-
Luka 14:12Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
12 Kenako anauzanso munthu amene anamuitana uja kuti: “Ukakonza chakudya chamasana kapena chamadzulo, usaitane mabwenzi ako, kapena abale ako, kapena afuko lako, kapena anthu olemera omwe amakhala nawe pafupi. Mwina nthawi ina iwonso angadzakuitane ndipo kudzakhala ngati kukubwezera.
-