LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • snnw nyimbo 150 tsa. 15
  • Kudzipeleka na Mtima Wonse

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kudzipeleka na Mtima Wonse
  • Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Nkhani Zofanana
  • Kudzipeleka na Mtima Wonse
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Munapeleka Mwana Wanu Wobadwa Yekha
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Umoyo wa Mpainiya
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
snnw nyimbo 150 tsa. 15

Nyimbo 150

Kudzipeleka na Mtima Wonse

Yopulinta

(Mateyu 9:37, 38)

  1. Yehova amatipatsa

    Zinthu zotisangalatsa.

    Afuna tisangalale

    Pamene timtumikila.

    (KOLASI)

    Mokondwa tifuna,

    kudzipeleka.

    Ndipo kulikonse,

    tipita mofunitsitsa.

  2. Kuno tili kuli nchito,

    Yofunika kuigwila.

    Tionetsa khama lathu,

    Pothandiza anthu onse.

    (KOLASI)

    Mokondwa tifuna,

    kudzipeleka.

    Ndipo kulikonse,

    tipita mofunitsitsa.

  3. Kulikonse kuli anthu,

    Na ku malo akutali.

    Tipita kukalengeza

    Uthenga kwa anthu onse.

    (KOLASI)

    Mokondwa tifuna,

    kudzipeleka.

    Ndipo kulikonse,

    tipita mofunitsitsa.

(Onaninso Yoh. 4:35; Mac. 2:8; Arom. 10:14.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2022)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2022 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani