LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 79
  • Aphunzitseni Kucilimika

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Aphunzitseni Kucilimika
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Aphunzitseni Kucilimika
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Moyo Ndi Wodabwitsa
    Imbirani Yehova
  • Moyo ni Cozizwitsa
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
Onaninso Zina
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 79

NYIMBO 79

Aphunzitseni Kucilimika

Yopulinta

(Mateyu 28:19, 20)

  1. 1. Tikondwa kuphunzitsa anthu

    Okonda coonadi.

    Onani mmene akulila

    M’njila ya coonadi.

    (KOLASI)

    Yehova, mvelani pempho

    Lakuti muŵasamale

    Mu dzina la Yesu Khristu

    Tipemphela akhale ocilimika.

  2. 2. Tinali kuŵapemphelela

    M’mavuto awo onse.

    Tinali kuŵasamalila.

    Yehova ‘wadalitsa.

    (KOLASI)

    Yehova, mvelani pempho

    Lakuti muŵasamale

    Mu dzina la Yesu Khristu

    Tipemphela akhale ocilimika.

  3. 3. Akhale odalila M’lungu,

    Na Mwana wake Yesu.

    Amvele ndipo apilile,

    Tifuna apambane.

    (KOLASI)

    Yehova, mvelani pempho

    Lakuti muŵasamale

    Mu dzina la Yesu Khristu

    Tipemphela akhale ocilimika.

(Onaninso Luka 6:48; Mac. 5:42; Afil. 4:1.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2022)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2022 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani