LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 82
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Onetsani Kuwala Kwanu”
    Imbirani Yehova
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 82

NYIMBO 82

“Onetsani Kuwala Kwanu”

Yopulinta

(Mateyu 5:16)

  1. 1. Yesu Mbuye wathu

    Analamula,

    Kuti tiwalitse

    Kuwala kwathu.

    Tiphunzitse ena

    Mau a M’lungu.

    Ndipo tiunikile

    Kuwala kwake.

  2. 2. Ise tilengeze

    Kwa anthu onse,

    Mau a Yehova

    Mulungu wathu.

    Ndipo tigaŵile

    Onse co’nadi,

    Tiŵaphunzitse onse

    Ofuna kumva.

  3. 3. Tikonde anansi

    Tiŵasamale.

    Makhalidwe athu

    Aunikile.

    Tidzakondweletsa

    Atate wathu,

    Ndipo tidzakhaladi

    Mabwenzi Ake.

(Onaninso Sal. 119:130; Mat. 5:14, 15, 45; Akol. 4:6.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2022)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2022 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani