LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 83
  • “Ku Nyumba ndi Nyumba”

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • “Ku Nyumba ndi Nyumba”
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • “Kunyumba Ndi Nyumba”
    Imbirani Yehova
  • Tilalikile Coonadi ca Ufumu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Tilalikire Choonadi cha Ufumu
    Imbirani Yehova
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 83

NYIMBO 83

“Ku Nyumba ndi Nyumba”

Yopulinta

(Machitidwe 20:20)

  1. 1. Mwa cimwemwe tilalika

    Ku nyumba ndi nyumba.

    Mu mizinda na mu midzi

    Konse timafika.

    Tilengeza za Ufumu

    Kwa onse pa dziko.

    Tiŵauza: “Yesu Khristu

    Tsopano ni Mfumu.”

  2. 2. Timalengeza kwa ena

    Za cipulumutso,

    Ca amene aitana

    Pa dzina la M’lungu.

    Koma ‘dzaitana bwanji

    Ngati samudziŵa?

    Conco tidzaŵadziŵitsa

    Dzina la Yehova.

  3. 3. Tiyeni tilalikile

    Ku nyumba ndi nyumba.

    Anthu asankhe kumvela

    Kapena kukana.

    Dzina la Mulungu wathu

    Tidzalilengeza.

    Tisaleke kulalika

    Ku nyumba ndi nyumba.

(Onaninso Mac. 2:21; Aroma 10:14.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2022)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2022 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani