LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 84
  • Kudzipeleka na Mtima Wonse

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kudzipeleka na Mtima Wonse
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Kudzipeleka na Mtima Wonse
    Imbilani Yehova—Nyimbo Zatsopano
  • Khalani ndi Moyo Wopambana
    Imbirani Yehova
  • Aphunzitseni Kucilimika
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 84

NYIMBO 84

Kudzipeleka na Mtima Wonse

Yopulinta

(Mateyu 9:37,38)

  1. 1. Yehova amatipatsa

    Zinthu zotisangalatsa.

    Afuna tisangalale

    Pamene titumikila.

    (KOLASI)

    Mokondwa tifuna,

    kudzipeleka.

    Ndipo kulikonse,

    tipita mofunitsitsa.

  2. 2. Kuno tili kuli nchito,

    Yofunika kuigwila.

    Tionetsa khama lathu,

    Pothandiza anthu onse.

    (KOLASI)

    Mokondwa tifuna,

    kudzipeleka.

    Ndipo kulikonse,

    tipita mofunitsitsa.

  3. 3. Kulikonse kuli anthu,

    Na ku malo akutali.

    Tipita kukalengeza

    Uthenga kwa anthu onse.

    (KOLASI)

    Mokondwa tifuna,

    kudzipeleka.

    Ndipo kulikonse,

    tipita mofunitsitsa.

(Onaninso Yoh. 4:35; Mac. 2:8; Aroma. 10:14.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2022)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2022 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani