LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • sjj nyimbo 96
  • Buku Lake la Mulungu ni Cuma

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Buku Lake la Mulungu ni Cuma
  • ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
  • Nkhani Zofanana
  • Buku la Mulungu Ndi Chuma Chamtengo Wapatali
    Imbirani Yehova
  • Funani Cipulumutso ca Mulungu
    ‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
‘Imbani Mokweza ndi Mosangalala’ kwa Yehova
sjj nyimbo 96

NYIMBO 96

Buku Lake la Mulungu ni Cuma

Yopulinta

(Miyambo 2:1)

  1. 1. Pali buku limene mau ake,

    Tikaŵelenga timakondwela.

    Mfundo zake zodabwitsa n’zamphamvu;

    Zimatipatsa ciyembekezo.

    Bukulo ndilo Baibo yoyela

    Analemba anauzilidwa.

    Anali amuna okonda M’lungu.

    Analemba mwa mphamvu ya mzimu.

  2. 2. Analemba nkhani za cilengedwe,

    Mmene M’lungu anacipangila.

    Analemba za moyo m’paradaiso

    Komanso mmene unasinthila.

    Analemba za mngelo wina wake

    Amene anatsutsa Yehova.

    Izi zinabweletsadi mavuto

    Koma Yehova adzapambana.

  3. 3. Lomba yafika nthawi tikondwele,

    Yesu wayamba kulamulila.

    Tilalikile uthenga wabwino

    Wonena za Ufumu wa M’lungu.

    M’buku lake muli zosangalatsa;

    Mulidi cakudya coculuka.

    Limatipatsa mtendele wambili.

    Tifunika tiziliŵelenga.

(Onaninso 2 Tim. 3:16; 2 Pet. 1:21.)

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2022)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2022 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani