LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • th phunzilo 4 tsa. 7
  • Kachulidwe ka Malemba Koyenela

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kachulidwe ka Malemba Koyenela
  • Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa
  • Nkhani Zofanana
  • Kumveketsa Bwino Cifukwa Coŵelengela Lemba
    Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa
  • Yesetsani Kuwafika pa Mtima Omvela
    Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa
  • Mawu Oyamba Ogwila Mtima
    Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa
Citani Khama pa Kuŵelenga na Kuphunzitsa
th phunzilo 4 tsa. 7

PHUNZILO 4

Kachulidwe ka Malemba Koyenela

Lemba losagwila mawu

Mateyu 22:41-45

ZOFUNIKILA: Konzekeletsani maganizo a omvela anu musanaŵelenge lemba.

MOCITILA:

  • Dziŵani cifukwa cimene mufuna kuŵelengela lembalo. Chulani lemba iliyonse mwa njila yokopa cidwi omvela anu ku mfundo yanu yofunika pa vesilo.

    Tumalangizo tothandizila

    Khalani na cithunzi ca nkhani yonse. Mukagwila mawu a munthu wina, chulani mwini wake weni-weni wa mawuwo, komanso mlembi weni-weni wa buku la m’Baibo.

  • Muzichula Baibo kuonetsa maziko a mfundo zanu. Pokamba na ŵanthu okhulupilila za Mulungu, muzichula Baibo kuti ni Mawu a Mulungu, poonetsa kuti ndilo gwelo la nzelu zopambana.

  • Kopelani cidwi pa lembalo. Funsani funso limene lembalo lidzayankha. Kapena chulani vuto limene lembalo lidzaonetsa molithetsela. Kapenanso chulani mfundo imene lembalo lidzawathandiza kuimvetsa.

    Tumalangizo tothandizila

    Ganizilani zimene omvela anu amazidziŵa kale pa nkhaniyo kapena pa lembalo. Chulani ngakhale lemba lodziŵika koma mwa njila yokopa cidwi, ndipo thandizani omvela anu kulimvetsa bwino.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2022)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2022 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani