-
Ezekieli 21:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Ndiyeno akakufunsa kuti, ‘N’chifukwa chiyani ukubuula?’+ Uwayankhe kuti, ‘N’chifukwa cha uthenga umene ndamva.’+ Pakuti uthengawo udzafika ndithu+ ndipo mtima wa munthu aliyense udzasungunuka ndi mantha.+ Anthu onse adzazizira nkhongono. Aliyense adzataya mtima ndipo mawondo onse adzachucha madzi.*+ ‘Uthengawo ufika ndithu+ ndipo zimene ukunena zidzachitikadi,’ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa.”
-