11 Kwa anthu inu, masomphenya a chilichonse akhala ngati mawu a m’buku limene lamatidwa kuti lisatsegulidwe,+ limene alipereka kwa munthu wodziwa kuwerenga, n’kumuuza kuti: “Werenga bukuli mokweza.” Koma iye n’kunena kuti: “Sindingathe kuliwerenga, chifukwa ndi lomatidwa.”+