-
Aisrayeli ndi Mitundu Yowazungulira‘Onani Dziko Lokoma’
-
-
Mulungu anauza Israyeli kuti ‘akachotse mitundu yaikulu’ isanu ndi iŵiri—Ahiti, Agirigasi, Aamori, Akanani, Aperizi, Ahivi, ndi Ayebusi—imene inayenera kuwonongedwa. Mitundu imeneyi inali ndi makhalidwe onyansa komanso chipembedzo chawo chinali choipa. Milungu yawo ina inali Baala (wotchuka ndi zipilala zamiyala zoimira mpheto ya mwamuna), Moleki (amene iwo anali kuperekako ana awo nsembe), ndi Asitaroti (Astarte) mulungu wamkazi wa kubala.—Deut. 7:1-4; 12:31; Eks. 23:23; Lev. 18:21-25; 20:2-5; Ower. 2:11-14; Sal. 106:37, 38.
-
-
Aisrayeli ndi Mitundu Yowazungulira‘Onani Dziko Lokoma’
-
-
E6 AHIVI
E7 AYEBUSI
-