Miyambo 12:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Kuli bwino kukhala munthu wamba koma n’kukhala ndi wantchito, kusiyana n’kukhala wodzikuza koma wopanda chakudya.+ Chivumbulutso 3:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Iwe ukunena kuti: “Ndine wolemera,+ ndapeza chuma chambiri ndipo sindikusowa kanthu,” koma sukudziwa kuti ndiwe wovutika, womvetsa chisoni, wosauka, wakhungu,+ ndi wamaliseche.
9 Kuli bwino kukhala munthu wamba koma n’kukhala ndi wantchito, kusiyana n’kukhala wodzikuza koma wopanda chakudya.+
17 Iwe ukunena kuti: “Ndine wolemera,+ ndapeza chuma chambiri ndipo sindikusowa kanthu,” koma sukudziwa kuti ndiwe wovutika, womvetsa chisoni, wosauka, wakhungu,+ ndi wamaliseche.