37 “Koma mukupitirizabe kukhala ndi moyo chifukwa anakonda makolo anu ndipo anasankha mbewu zawo zobwera pambuyo pawo,+ ndi kukutulutsani mu Iguputo ndi mphamvu zake zazikulu,+ komanso anali kukuyang’anirani.
15 Koma Yehova anadziphatika kwa makolo anu ndi kuwakonda, moti anasankha ana awo obadwa m’mbuyo mwawo,+ inuyo, pakati pa anthu onse monga mmene zilili lero.